Yesaya 45
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
45 Yehova akuyankhula ndi wodzozedwa wake
Koresi amene anamugwira dzanja lamanja
kuti agonjetse mitundu ya anthu
ndi kuwalanda mafumu zida zawo zankhondo,
ndi kutsekula zitseko
kuti zipatazo zisadzatsekedwenso ndi ichi:
2 Ine ndidzayenda patsogolo pako,
ndi kusalaza mapiri;
ndidzaphwanya zitseko za mkuwa
ndi kuthyola mipiringidzo ya chitsulo.
3 Ndidzakupatsa chuma chobisika mu mdima,
katundu wa pamalo obisika,
kotero kuti udziwe kuti Ine ndine Yehova
Mulungu wa Israeli, amene ndakuyitana pokutchula dzina.
4 Chifukwa cha mtumiki wanga Yakobo,
chifukwa cha wosankhidwa wanga Israeli,
Ine ndakuyitana pokutchula dzina
ndipo ndakupatsa dzina laulemu
ngakhale iwe sukundidziwa Ine.
5 Ine ndine Yehova ndipo palibenso wina;
kupatula Ine palibenso Mulungu wina.
Ndidzakupatsa mphamvu,
ngakhale sukundidziwa Ine,
6 kotero kuti kuchokera kummawa mpaka kumadzulo
anthu adzadziwa kuti palibe wina koma Ine ndekha.
Ine ndine Yehova,
ndipo palibenso wina.
7 Ndimalenga kuwala ndi mdima,
ndimabweretsa madalitso ndi tsoka;
ndine Yehova, amene ndimachita zonsezi.
8 “Iwe thambo gwetsa mvula kuchokera kumwamba;
mitambo ivumbwe mivumbi ya chilungamo.
Dziko lapansi litsekuke,
ndipo chipulumutso chiphuke kuti
chilungamo chimereponso;
Ine Yehova, ndine ndalenga zimenezi.
9 “Tsoka kwa wokangana ndi mlengi wake,
ngakhale kuti ali ngati phale chabe pakati pa mapale anzake.
Kodi dongo lingafunse munthu wowumba kuti,
‘Kodi ukuwumba chiyani?’
Kodi ntchito yako inganene kuti,
‘Ulibe luso?’
10 Tsoka kwa wofunsa abambo ake kuti,
‘Kodi munabereka chiyani?’
Kapena amayi ake kuti,
‘Kodi mufuna kubereka chiyani?’
11 “Yehova
Woyerayo wa Israeli, ndiponso Mlengi wake akunena,
zokhudza zinthu zimene zikubwera ndi izi:
Kodi iwe ukundifunsa za ana anga,
kapena kundilamula pa zokhudza ntchito zanga?
12 Ndine amene ndinapanga dziko lapansi
ndikulenga munthu kuti akhalemo.
Ine ndi manja anga ndinayalika thambo;
ndimalamulira zolengedwa zonse za mlengalenga.
13 Ndine amene ndidzawutsa Koresi kuti chilungamo changa chikwaniritsidwe:
ndipo ndidzawongolera njira zake zonse.
Iye adzamanganso mzinda wanga
ndi kumasula anthu anga amene ali mu ukapolo,
wopanda kupereka ndalama kapena mphotho,
akutero Yehova Wamphamvuzonse.”
14 Yehova akuti,
“Chuma cha ku Igupto ndi chuma cha malonda cha Kusi chidzakhala chanu.
Anthu amphamvu zawo ndi athanzi a ku Seba
adzabwera kwa inu
ndipo adzakhala anthu anu;
iwo adzidzakutsatani pambuyo panu
ali mʼmaunyolo.
Adzakugwadirani
ndi kukupemphani, ponena kuti,
‘Ndithudi Mulungu ali ndi inu, ndipo palibenso wina;
palibenso mulungu wina.’ ”
15 Zoonadi inu muli ndi Mulungu wobisika
amene ali Mulungu ndi Mpulumutsi wa Israeli.
16 Onse amene amapanga mafano adzawachititsa manyazi ndi kuwanyozetsa.
Adzakhala osokonezeka maganizo.
17 Koma Yehova adzapulumutsa Israeli
ndi chipulumutso chamuyaya;
simudzachitanso manyazi kapena kunyozeka
mpaka kalekale.
18 Yehova
analenga zinthu zakumwamba,
Iye ndiye Mulungu;
amene akulenga dziko lapansi,
ndi kulikhazikitsa,
sanalipange kuti likhale lopanda kanthu,
koma analipanga kuti anthu akhalemo.
Iyeyu akunena kuti:
Ine ndine Yehova,
ndipo palibenso wina.
19 Ine sindinayankhule mwachinsinsi,
pamalo ena a mdima;
Ine sindinaziwuze zidzukulu za Yakobo kuti,
“Ndifunefuneni ku malo kopanda kanthu.”
Ine Yehova, ndimayankhula zoona;
ndikunena zolungama.
20 Yehova akuti, “Sonkhanani pamodzi ndipo mubwere;
yandikirani, inu amene munapulumuka pothawa nkhondo kwa anthu a mitundu ina.
Ndinu opanda nzeru amene mumanyamula mafano a mitengo,
amene mumapemphera kwa milungu imene singathe kupulumutsa.
21 Fotokozani mlandu wanu,
mupatsane nzeru nonse pamodzi.
Kodi ndani ananeneratu zimenezi kalekale?
Ndani anazifotokozeratu zimenezi nthawi yamakedzana?
Kodi si Ineyo Yehova?
Ndipo palibenso Mulungu wina kupatula Ine,
Mulungu wolungama ndi Wopulumutsa,
palibenso wina kupatula Ine.
22 “Tembenukirani kwa Ine kuti mupulumuke,
inu anthu onse a pa dziko lapansi,
pakuti Ine ndine Mulungu ndipo palibenso wina.
23 Ndalumbira ndekha,
pakamwa panga patulutsa mawu owona,
mawu amene sadzasinthika konse akuti,
bondo lililonse lidzagwada pamaso panga;
anthu onse adzalumbira potchula dzina langa.
24 Iwo adzanene kwa Ine kuti,
‘Chilungamo ndi mphamvu zimapezeka mwa Yehova yekha.’ ”
Onse amene anamuwukira Iye
adzabwera kwa Iye ndipo adzachita manyazi.
25 Koma mwa Yehova zidzukulu zonse za Israeli
zidzapambana ndi kupeza ulemerero.
Isaiah 45
New International Version
45 “This is what the Lord says to his anointed,(A)
to Cyrus,(B) whose right hand I take hold(C) of
to subdue nations(D) before him
and to strip kings of their armor,
to open doors before him
so that gates will not be shut:
2 I will go before you(E)
and will level(F) the mountains[a];
I will break down gates(G) of bronze
and cut through bars of iron.(H)
3 I will give you hidden treasures,(I)
riches stored in secret places,(J)
so that you may know(K) that I am the Lord,
the God of Israel, who summons you by name.(L)
4 For the sake of Jacob my servant,(M)
of Israel my chosen,
I summon you by name
and bestow on you a title of honor,
though you do not acknowledge(N) me.
5 I am the Lord, and there is no other;(O)
apart from me there is no God.(P)
I will strengthen you,(Q)
though you have not acknowledged me,
6 so that from the rising of the sun
to the place of its setting(R)
people may know(S) there is none besides me.(T)
I am the Lord, and there is no other.
7 I form the light and create darkness,(U)
I bring prosperity and create disaster;(V)
I, the Lord, do all these things.
8 “You heavens above, rain(W) down my righteousness;(X)
let the clouds shower it down.
Let the earth open wide,
let salvation(Y) spring up,
let righteousness flourish with it;
I, the Lord, have created it.
9 “Woe to those who quarrel(Z) with their Maker,(AA)
those who are nothing but potsherds(AB)
among the potsherds on the ground.
Does the clay say to the potter,(AC)
‘What are you making?’(AD)
Does your work say,
‘The potter has no hands’?(AE)
10 Woe to the one who says to a father,
‘What have you begotten?’
or to a mother,
‘What have you brought to birth?’
11 “This is what the Lord says—
the Holy One(AF) of Israel, and its Maker:(AG)
Concerning things to come,
do you question me about my children,
or give me orders about the work of my hands?(AH)
12 It is I who made the earth(AI)
and created mankind on it.
My own hands stretched out the heavens;(AJ)
I marshaled their starry hosts.(AK)
13 I will raise up Cyrus[b](AL) in my righteousness:
I will make all his ways straight.(AM)
He will rebuild my city(AN)
and set my exiles free,
but not for a price or reward,(AO)
says the Lord Almighty.”
14 This is what the Lord says:
“The products(AP) of Egypt and the merchandise of Cush,[c]
and those tall Sabeans(AQ)—
they will come over to you(AR)
and will be yours;
they will trudge behind you,(AS)
coming over to you in chains.(AT)
They will bow down before you
and plead(AU) with you, saying,
‘Surely God is with you,(AV) and there is no other;
there is no other god.(AW)’”
15 Truly you are a God who has been hiding(AX) himself,
the God and Savior(AY) of Israel.
16 All the makers of idols will be put to shame and disgraced;(AZ)
they will go off into disgrace together.
17 But Israel will be saved(BA) by the Lord
with an everlasting salvation;(BB)
you will never be put to shame or disgraced,(BC)
to ages everlasting.
18 For this is what the Lord says—
he who created the heavens,
he is God;
he who fashioned and made the earth,(BD)
he founded it;
he did not create it to be empty,(BE)
but formed it to be inhabited(BF)—
he says:
“I am the Lord,
and there is no other.(BG)
19 I have not spoken in secret,(BH)
from somewhere in a land of darkness;(BI)
I have not said to Jacob’s descendants,(BJ)
‘Seek(BK) me in vain.’
I, the Lord, speak the truth;
I declare what is right.(BL)
20 “Gather together(BM) and come;
assemble, you fugitives from the nations.
Ignorant(BN) are those who carry(BO) about idols of wood,
who pray to gods that cannot save.(BP)
21 Declare what is to be, present it—
let them take counsel together.
Who foretold(BQ) this long ago,
who declared it from the distant past?(BR)
Was it not I, the Lord?
And there is no God apart from me,(BS)
a righteous God(BT) and a Savior;(BU)
there is none but me.
22 “Turn(BV) to me and be saved,(BW)
all you ends of the earth;(BX)
for I am God, and there is no other.(BY)
23 By myself I have sworn,(BZ)
my mouth has uttered in all integrity(CA)
a word that will not be revoked:(CB)
Before me every knee will bow;(CC)
by me every tongue will swear.(CD)
24 They will say of me, ‘In the Lord alone
are deliverance(CE) and strength.(CF)’”
All who have raged against him
will come to him and be put to shame.(CG)
25 But all the descendants(CH) of Israel
will find deliverance(CI) in the Lord
and will make their boast in him.(CJ)
Footnotes
- Isaiah 45:2 Dead Sea Scrolls and Septuagint; the meaning of the word in the Masoretic Text is uncertain.
- Isaiah 45:13 Hebrew him
- Isaiah 45:14 That is, the upper Nile region
Isaiah 45
King James Version
45 Thus saith the Lord to his anointed, to Cyrus, whose right hand I have holden, to subdue nations before him; and I will loose the loins of kings, to open before him the two leaved gates; and the gates shall not be shut;
2 I will go before thee, and make the crooked places straight: I will break in pieces the gates of brass, and cut in sunder the bars of iron:
3 And I will give thee the treasures of darkness, and hidden riches of secret places, that thou mayest know that I, the Lord, which call thee by thy name, am the God of Israel.
4 For Jacob my servant's sake, and Israel mine elect, I have even called thee by thy name: I have surnamed thee, though thou hast not known me.
5 I am the Lord, and there is none else, there is no God beside me: I girded thee, though thou hast not known me:
6 That they may know from the rising of the sun, and from the west, that there is none beside me. I am the Lord, and there is none else.
7 I form the light, and create darkness: I make peace, and create evil: I the Lord do all these things.
8 Drop down, ye heavens, from above, and let the skies pour down righteousness: let the earth open, and let them bring forth salvation, and let righteousness spring up together; I the Lord have created it.
9 Woe unto him that striveth with his Maker! Let the potsherd strive with the potsherds of the earth. Shall the clay say to him that fashioneth it, What makest thou? or thy work, He hath no hands?
10 Woe unto him that saith unto his father, What begettest thou? or to the woman, What hast thou brought forth?
11 Thus saith the Lord, the Holy One of Israel, and his Maker, Ask me of things to come concerning my sons, and concerning the work of my hands command ye me.
12 I have made the earth, and created man upon it: I, even my hands, have stretched out the heavens, and all their host have I commanded.
13 I have raised him up in righteousness, and I will direct all his ways: he shall build my city, and he shall let go my captives, not for price nor reward, saith the Lord of hosts.
14 Thus saith the Lord, The labour of Egypt, and merchandise of Ethiopia and of the Sabeans, men of stature, shall come over unto thee, and they shall be thine: they shall come after thee; in chains they shall come over, and they shall fall down unto thee, they shall make supplication unto thee, saying, Surely God is in thee; and there is none else, there is no God.
15 Verily thou art a God that hidest thyself, O God of Israel, the Saviour.
16 They shall be ashamed, and also confounded, all of them: they shall go to confusion together that are makers of idols.
17 But Israel shall be saved in the Lord with an everlasting salvation: ye shall not be ashamed nor confounded world without end.
18 For thus saith the Lord that created the heavens; God himself that formed the earth and made it; he hath established it, he created it not in vain, he formed it to be inhabited: I am the Lord; and there is none else.
19 I have not spoken in secret, in a dark place of the earth: I said not unto the seed of Jacob, Seek ye me in vain: I the Lord speak righteousness, I declare things that are right.
20 Assemble yourselves and come; draw near together, ye that are escaped of the nations: they have no knowledge that set up the wood of their graven image, and pray unto a god that cannot save.
21 Tell ye, and bring them near; yea, let them take counsel together: who hath declared this from ancient time? who hath told it from that time? have not I the Lord? and there is no God else beside me; a just God and a Saviour; there is none beside me.
22 Look unto me, and be ye saved, all the ends of the earth: for I am God, and there is none else.
23 I have sworn by myself, the word is gone out of my mouth in righteousness, and shall not return, That unto me every knee shall bow, every tongue shall swear.
24 Surely, shall one say, in the Lord have I righteousness and strength: even to him shall men come; and all that are incensed against him shall be ashamed.
25 In the Lord shall all the seed of Israel be justified, and shall glory.
The Word of God in Contemporary Chichewa Copyright © 2002, 2016 by Biblica, Inc.® Used by permission of Biblica, Inc.® All rights reserved worldwide. Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero Mwini © 2002, 2016 ndi Biblica, Inc.® Kugwiritsa ntchito mwachilolezo. Umwini ndi otetezedwa pa dziko lonse.
Holy Bible, New International Version®, NIV® Copyright ©1973, 1978, 1984, 2011 by Biblica, Inc.® Used by permission. All rights reserved worldwide.
NIV Reverse Interlinear Bible: English to Hebrew and English to Greek. Copyright © 2019 by Zondervan.