Add parallel Print Page Options

Salimo la ana a Kora. Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Potsata mayimbidwe a nyimbo yoti: “Pa Matenda ndi pa Mazunzo.” Ndakatulo ya Hemani, wa banja la Ezara.

88 Inu Yehova, Mulungu amene mumandipulumutsa,
    usana ndi usiku ndimalira pamaso panu.

Read full chapter