Miyambo 14
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
14 Mkazi wanzeru amamanga banja lake,
koma mkazi wopusa amalimasula ndi manja ake omwe.
2 Amene amayenda molungama amaopa Yehova,
koma amene njira zake ndi zoyipa amanyoza Yehova.
3 Kuyankhula kwa chitsiru kumamuyitanira ndodo pa msana,
koma milomo ya munthu wanzeru imamuteteza.
4 Pakasowa ngʼombe zolima gome limakhala lopanda chakudya,
koma pakakhala ngʼombe zamphamvu zakudya zimachulukanso.
5 Mboni yokhulupirika sinama,
koma mboni yonyenga imayankhula zabodza.
6 Wonyoza anzake amafunafuna nzeru koma osayipeza,
koma munthu womvetsa bwino amadziwa zinthu msanga.
7 Khala kutali ndi munthu wopusa
chifukwa sudzapeza mawu a nzeru.
8 Nzeru za munthu wochenjera zagona pakuzindikira njira zake.
Koma uchitsiru wa zitsiru umapusitsidwa ndi chinyengo chawo chomwe.
9 Zitsiru zimanyoza za kulapa machimo, awo,
koma kufuna kwabwino kumapezeka mwa anthu olungama.
10 Mtima uliwonse umadziwa wokha zowawa zake,
ndipo palibe wina aliyense angadziwe kukondwa kwake.
11 Nyumba ya munthu woyipa idzapasuka,
koma tenti ya munthu wowongoka mtima idzakhazikika.
12 Pali njira ina yooneka ngati yabwino kwa munthu,
koma kumatsiriziro kwake ndi ku imfa.
13 Ngakhale poseka mtima utha kumva kuwawa,
ndipo mathero achimwemwe akhoza kukhala chisoni.
14 Munthu wosakhulupirika adzalandira zogwirizana ndi ntchito yake,
koma munthu wabwino adzalandira mphotho ya ntchito yake.
15 Munthu wopusa amakhulupirira chilichonse,
koma munthu wochenjera amaganizira bwino mayendedwe ake.
16 Munthu wanzeru amaopa Mulungu ndipo amapewa zoyipa,
koma munthu wopusa ndi wokula mtima amakhala wosasamala.
17 Munthu wopsa mtima msanga amachita zinthu za uchitsiru,
ndipo anthu amadana ndi munthu wachinyengo.
18 Anthu opusa amalandira uchitsiru,
koma anthu ochenjera amavekedwa chipewa cha ulemerero wa kudziwa zinthu.
19 Anthu oyipa adzagwada pamaso pa anthu abwino,
ndipo anthu oyipa adzapempha thandizo kwa anthu olungama.
20 Munthu wosauka ngakhale anansi ake omwe amamuda,
koma munthu wolemera ali ndi abwenzi ambiri.
21 Wonyoza mnansi wake ndi wochimwa
koma ndi wodala amene amachitira chifundo anthu osowa.
22 Kodi amene amakonzekera zoyipa sasochera?
Koma amene amakonzekera zabwino anthu amawaonetsa chikondi ndi kukhulupirika.
23 Ntchito iliyonse imakhala ndi phindu,
koma kuyankhulayankhula kumabweretsa umphawi.
24 Chipewa chaulemu cha anthu a nzeru ndi chuma chawo chomwe,
koma malipiro a zitsiru ndi uchitsiru.
25 Mboni yokhulupirika imapulumutsa miyoyo,
koma mboni yabodza imaphetsa.
26 Amene amaopa Yehova ali ndi chitetezo chokwanira
ndipo iye adzakhala pothawira pa ana ake.
27 Kuopa Yehova ndiye kasupe wamoyo,
kumathandiza munthu kuti apewe msampha wa imfa.
28 Gulu lalikulu la anthu ndiye ulemerero wa mfumu,
koma popanda anthu kalonga amawonongeka.
29 Munthu wosapsa mtima msanga amamvetsa zinthu kwambiri,
koma munthu wopsa mtima msanga amaonetsa uchitsiru wake.
30 Mtima wodekha umapatsa thupi moyo,
koma nsanje imawoletsa mafupa.
31 Amene amapondereza mʼmphawi amanyoza mlengi wake,
koma wochitira chifundo munthu wosowa amalemekeza Mulungu.
32 Anthu oyipa adzakanthidwa chifukwa cha ntchito zawo zomwe,
koma olungama adzatetezedwa mwa imfa yawo.
33 Nzeru zimakhala mu mtima mwa anthu omvetsa zinthu,
koma nzeru sipezeka mu mtima mwa zitsiru.
34 Chilungamo chimakweza mtundu wa anthu,
koma uchimo umachititsa manyazi mtundu uliwonse.
35 Mfumu imasangalatsidwa ndi wantchito wanzeru,
koma imachitira ukali wantchito wochititsa manyazi.
Proverbs 14
Holman Christian Standard Bible
2 Whoever lives with integrity fears the Lord,(C)
but the one who is devious in his ways despises Him.(D)
3 The proud speech of a fool brings a rod of discipline,[a]
but the lips of the wise protect them.(E)
4 Where there are no oxen, the feeding trough is empty,[b]
but an abundant harvest comes
through the strength of an ox.
5 An honest witness does not deceive,
but a dishonest witness utters lies.(F)
6 A mocker seeks wisdom and doesn’t find it,
but knowledge comes easily to the perceptive.
7 Stay away from a foolish man;
you will gain no knowledge from his speech.(G)
8 The sensible man’s wisdom is to consider his way,
but the stupidity of fools deceives them.
9 Fools mock at making restitution,[c]
but there is goodwill among the upright.
10 The heart knows its own bitterness,
and no outsider shares in its joy.
13 Even in laughter a heart may be sad,
and joy may end in grief.(K)
14 The disloyal one will get what his conduct deserves,
and a good man, what his deeds deserve.(L)
17 A quick-tempered man acts foolishly,
and a man who schemes is hated.(O)
18 The inexperienced inherit foolishness,
but the sensible are crowned with knowledge.
19 The evil bow before those who are good,
the wicked, at the gates of the righteous.
21 The one who despises his neighbor sins,(R)
but whoever shows kindness to the poor will be happy.(S)
24 The crown of the wise is their wealth,
but the foolishness of fools produces foolishness.
25 A truthful witness rescues lives,
but one who utters lies is deceitful.(W)
26 In the fear of the Lord one has strong confidence
and his children have a refuge.(X)
27 The fear of the Lord is a fountain of life,
turning people away from the snares of death.(Y)
28 A large population is a king’s splendor,
but a shortage of people is a ruler’s devastation.
29 A patient person shows great understanding,(Z)
but a quick-tempered one promotes foolishness.
31 The one who oppresses the poor person insults his Maker,(AC)
but one who is kind to the needy honors Him.(AD)
32 The wicked one is thrown down by his own sin,(AE)
but the righteous one has a refuge in his death.(AF)
34 Righteousness exalts a nation,
but sin is a disgrace to any people.(AH)
35 A king favors a wise servant,(AI)
but his anger falls on a disgraceful one.
Footnotes
- Proverbs 14:3 Some emend to In the mouth of a fool is a rod for his back
- Proverbs 14:4 Or clean
- Proverbs 14:9 Or at guilt offerings
- Proverbs 14:11 Lit flourish
- Proverbs 14:15 Lit the prudent understand
- Proverbs 14:16 Or and falls
- Proverbs 14:23 Lit but word of lips
- Proverbs 14:33 LXX reads unknown
Proverbios 14
Dios Habla Hoy
14 La mujer sabia construye su casa;
la necia, con sus propias manos la destruye.
2 El de recta conducta honra al Señor;
el de conducta torcida lo desprecia.
3 De la boca del necio brota el orgullo;
de los labios del sabio, su protección.
4 Cuando no hay bueyes, el trigo falta;
con la fuerza del buey, la cosecha aumenta.
5 El testigo verdadero no miente;
el testigo falso dice mentiras.
6 El insolente busca sabiduría y no la encuentra;
para el inteligente, el saber es cosa fácil.
7 Aléjate del necio,
pues de sus labios no obtendrás conocimiento.
8 La sabiduría hace al sabio entender su conducta,
pero al necio lo engaña su propia necedad.
9 Los necios se burlan de sus culpas,
pero entre los hombres honrados hay buena voluntad.
10 El corazón conoce sus propias amarguras,
y no comparte sus alegrías con ningún extraño.
11 La casa de los malvados será destruida;
la de los hombres honrados prosperará.
12 Hay caminos que parecen derechos,
pero al final de ellos está la muerte.
13 Hasta de reírse duele el corazón,
y al final la alegría acaba en llanto.
14 El necio está satisfecho de su conducta;
el hombre bueno lo está de sus acciones.
15 El imprudente cree todo lo que le dicen;
el prudente se fija por dónde anda.
16 El sabio teme al mal y se aparta de él,
pero al necio nada parece importarle.
17 El que es impulsivo actúa sin pensar;
el que es reflexivo mantiene la calma.
18 Los imprudentes son herederos de la necedad;
los prudentes se rodean de conocimientos.
19 Los malvados se inclinarán ante los buenos;
los malos suplicarán a las puertas de los justos.
20 Al pobre, hasta sus propios amigos lo odian;
al rico le sobran amigos.
21 El que desprecia a su amigo comete un pecado,
pero ¡feliz aquel que se compadece del pobre!
22 Los que buscan hacer lo malo, pierden el camino;
los que buscan hacer lo bueno son objeto de amor y lealtad.
23 De todo esfuerzo se saca provecho;
del mucho hablar, sólo miseria.
24 La corona del sabio es su inteligencia;
la de los necios, su necedad.
25 El testigo verdadero salva a otros la vida;
el testigo falso es causa de muerte.
26 El honrar al Señor es una firme esperanza
que da seguridad a los hijos.
27 El honrar al Señor es fuente de vida
que libra de los lazos de la muerte.
28 Gobernar a muchos es una honra para el rey;
gobernar a pocos es su ruina.
29 Ser paciente es muestra de mucha inteligencia;
ser impaciente es muestra de gran estupidez.
30 La mente tranquila es vida para el cuerpo,
pero la envidia corroe hasta los huesos.
31 Ofende a su Creador quien oprime al pobre,
pero lo honra quien le tiene compasión.
32 Al malvado lo arruina su propia maldad;
al hombre honrado lo protege su honradez.
33 La sabiduría habita en mentes que razonan,
pero entre los necios es desconocida.
34 La justicia es el orgullo de una nación;
el pecado es su vergüenza.
35 El siervo capaz se gana el favor del rey,
pero el incapaz se gana su enojo.
The Word of God in Contemporary Chichewa Copyright © 2002, 2016 by Biblica, Inc.® Used by permission of Biblica, Inc.® All rights reserved worldwide. Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero Mwini © 2002, 2016 ndi Biblica, Inc.® Kugwiritsa ntchito mwachilolezo. Umwini ndi otetezedwa pa dziko lonse.
Copyright © 1999, 2000, 2002, 2003, 2009 by Holman Bible Publishers, Nashville Tennessee. All rights reserved.
Dios habla hoy ®, © Sociedades Bíblicas Unidas, 1966, 1970, 1979, 1983, 1996.