Mateyu 4:24
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
24 Mbiri yake yonse inawanda ku Siriya konse ndipo anthu anabweretsa kwa Iye onse amene anali odwala nthenda zosiyanasiyana, womva maululu aakulu, ogwidwa ndi ziwanda, odwala matenda akugwa ndi olumala ndipo Iye anawachiritsa.
Read full chapter
Matthew 4:24
New International Version
24 News about him spread all over Syria,(A) and people brought to him all who were ill with various diseases, those suffering severe pain, the demon-possessed,(B) those having seizures,(C) and the paralyzed;(D) and he healed them.
Mateyu 17:15
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
15 Iye anati, “Ambuye, muchitireni chifundo mwana wanga akudwala matenda akugwa ndipo akuvutika kwambiri. Kawirikawiri iye amagwa pa moto kapena mʼmadzi.
Read full chapter
Matthew 17:15
New International Version
15 “Lord, have mercy on my son,” he said. “He has seizures(A) and is suffering greatly. He often falls into the fire or into the water.
The Word of God in Contemporary Chichewa Copyright © 2002, 2016 by Biblica, Inc.® Used by permission of Biblica, Inc.® All rights reserved worldwide. Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero Mwini © 2002, 2016 ndi Biblica, Inc.® Kugwiritsa ntchito mwachilolezo. Umwini ndi otetezedwa pa dziko lonse.
Holy Bible, New International Version®, NIV® Copyright ©1973, 1978, 1984, 2011 by Biblica, Inc.® Used by permission. All rights reserved worldwide.
NIV Reverse Interlinear Bible: English to Hebrew and English to Greek. Copyright © 2019 by Zondervan.