Add parallel Print Page Options

24 Mbiri yake yonse inawanda ku Siriya konse ndipo anthu anabweretsa kwa Iye onse amene anali odwala nthenda zosiyanasiyana, womva maululu aakulu, ogwidwa ndi ziwanda, odwala matenda akugwa ndi olumala ndipo Iye anawachiritsa.

Read full chapter

24 News about him spread all over Syria,(A) and people brought to him all who were ill with various diseases, those suffering severe pain, the demon-possessed,(B) those having seizures,(C) and the paralyzed;(D) and he healed them.

Read full chapter

15 Iye anati, “Ambuye, muchitireni chifundo mwana wanga akudwala matenda akugwa ndipo akuvutika kwambiri. Kawirikawiri iye amagwa pa moto kapena mʼmadzi.

Read full chapter

15 “Lord, have mercy on my son,” he said. “He has seizures(A) and is suffering greatly. He often falls into the fire or into the water.

Read full chapter