Add parallel Print Page Options

Salimo la Davide. Atathawa mwana wake Abisalomu.

Inu Yehova, achulukadi adani anga!
    Achulukadi amene andiwukira!
Ambiri akunena za ine kuti,
    “Mulungu sadzamupulumutsa.”
            Sela

Koma Inu Yehova, ndinu chishango chonditeteza,
    Inu mwandiveka ulemerero ndipo mwanditukula.
Kwa Yehova, Ine ndilira mofuwula
    ndipo Iye amandiyankha kuchokera ku phiri lake loyera.
            Sela

Ine ndimagona ndi kupeza tulo;
    ndimadzukanso chifukwa Yehova amandichirikiza.
Sindidzaopa adani anga osawerengeka amene
    abwera kulimbana nane kuchokera ku madera onse.

Dzukani, Inu Yehova!
    Pulumutseni, Inu Mulungu wanga.
Akantheni adani anga onse pa msagwada;
    gululani mano a anthu oyipa.

Chipulumutso chimachokera kwa Yehova.
    Madalitso akhale pa anthu anu.
            Sela

Psalm 3[a]

A psalm of David. When he fled from his son Absalom.(A)

Lord, how many are my foes!
    How many rise up against me!
Many are saying of me,
    “God will not deliver him.(B)[b]

But you, Lord, are a shield(C) around me,
    my glory, the One who lifts my head high.(D)
I call out to the Lord,(E)
    and he answers me from his holy mountain.(F)

I lie down and sleep;(G)
    I wake again,(H) because the Lord sustains me.
I will not fear(I) though tens of thousands
    assail me on every side.(J)

Arise,(K) Lord!
    Deliver me,(L) my God!
Strike(M) all my enemies on the jaw;
    break the teeth(N) of the wicked.

From the Lord comes deliverance.(O)
    May your blessing(P) be on your people.

Footnotes

  1. Psalm 3:1 In Hebrew texts 3:1-8 is numbered 3:2-9.
  2. Psalm 3:2 The Hebrew has Selah (a word of uncertain meaning) here and at the end of verses 4 and 8.