Job 4:8
New International Version
Yobu 4:8
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
8 Monga ndaonera ine, anthu amene amatipula zoyipa,
ndi iwo amene amadzala mavuto, amakolola zomwezo.
Job 20:11
New International Version
Yobu 20:11
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
11 Mphamvu zaunyamata zimene zili mʼthupi mwake
zidzagona naye limodzi mʼfumbi.
Proverbs 1:31
New International Version
31 they will eat the fruit of their ways
and be filled with the fruit of their schemes.(A)
Miyambo 1:31
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
31 Tsono adzadya zipatso zoyenera mayendedwe awo
ndi kukhuta ndi ntchito zimene anachita kwa ena.
Holy Bible, New International Version®, NIV® Copyright ©1973, 1978, 1984, 2011 by Biblica, Inc.® Used by permission. All rights reserved worldwide.
NIV Reverse Interlinear Bible: English to Hebrew and English to Greek. Copyright © 2019 by Zondervan.
The Word of God in Contemporary Chichewa Copyright © 2002, 2016 by Biblica, Inc.® Used by permission of Biblica, Inc.® All rights reserved worldwide. Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero Mwini © 2002, 2016 ndi Biblica, Inc.® Kugwiritsa ntchito mwachilolezo. Umwini ndi otetezedwa pa dziko lonse.
