As I have observed,(A) those who plow evil(B)
    and those who sow trouble reap it.(C)

Read full chapter

Monga ndaonera ine, anthu amene amatipula zoyipa,
    ndi iwo amene amadzala mavuto, amakolola zomwezo.

Read full chapter

11 The youthful vigor(A) that fills his bones(B)
    will lie with him in the dust.(C)

Read full chapter

11 Mphamvu zaunyamata zimene zili mʼthupi mwake
    zidzagona naye limodzi mʼfumbi.

Read full chapter

31 they will eat the fruit of their ways
    and be filled with the fruit of their schemes.(A)

Read full chapter

31 Tsono adzadya zipatso zoyenera mayendedwe awo
    ndi kukhuta ndi ntchito zimene anachita kwa ena.

Read full chapter