Add parallel Print Page Options

Monga ndaonera ine, anthu amene amatipula zoyipa,
    ndi iwo amene amadzala mavuto, amakolola zomwezo.

Read full chapter

11 Mphamvu zaunyamata zimene zili mʼthupi mwake
    zidzagona naye limodzi mʼfumbi.

Read full chapter

31 Tsono adzadya zipatso zoyenera mayendedwe awo
    ndi kukhuta ndi ntchito zimene anachita kwa ena.

Read full chapter