1 Mbiri 2
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
Ana a Israeli
2 Ana a Israeli anali awa:
Rubeni, Simeoni, Levi, Yuda, Isakara, Zebuloni, 2 Dani, Yosefe, Benjamini, Nafutali, Gadi ndi Aseri.
Yuda Mpaka pa Ana a Hezironi
Ana a Hezironi
3 Ana a Yuda anali awa:
Eri, Onani ndi Sela. Ana atatu awa anabereka ndi mkazi wa Chikanaani, Batisuwa. Eri, mwana woyamba wa Yuda anali woyipa kwambiri pamaso pa Yehova, kotero Yehova anamupha. 4 Mpongozi wake Tamara anamuberekera Perezi ndi Zera. Ana onse a Yuda analipo asanu.
5 Ana a Perezi anali awa:
Hezironi ndi Hamuli.
6 Ana a Zera anali awa:
Zimuri, Etani, Hemani, Kalikoli ndi Dara. Onse analipo asanu.
7 Mwana wa Karimi anali
Akani, amene anabweretsa mavuto pakati pa Israeli pamene anatenga zinthu zoyenera kuwonongedwa.
8 Mwana wa Etani anali
Azariya.
9 Ana amene anabadwa kwa Hezironi anali:
Yerahimeeli, Ramu ndi Kelubai.
Kuchokera kwa Ramu Mwana wa Hezironi
10 Ramu anabereka
Aminadabu ndipo Aminadabu anali abambo ake a Naasoni, mtsogoleri wa fuko la Yuda. 11 Naasoni anabereka Salima, Salima anabereka Bowazi, 12 Bowazi anabereka Obedi ndipo Obedi anabereka Yese.
13 Yese anabereka
Eliabu mwana wake woyamba, wachiwiri Abinadabu, wachitatu Simea, 14 wachinayi Netaneli, wachisanu Radai, 15 wachisanu ndi chimodzi Ozemu ndi wachisanu ndi chiwiri Davide. 16 Alongo awo anali Zeruya ndi Abigayeli. Ana atatu a Zeruya anali Abisai Yowabu ndi Asaheli. 17 Abigayeli anali amayi ake a Amasa amene abambo ake anali Yeteri wa fuko la Ismaeli.
Kalebe Mwana wa Hezironi
18 Kalebe mwana wa Hezironi anabereka ana mwa Azuba mkazi wake (ndi mwa Yerioti). Ana a mkaziyo anali awa: Yeseri, Sobabu ndi Aridoni. 19 Azuba atamwalira, Kalebe anakwatira Efurata, amene anamuberekera Huri. 20 Huri anabereka Uri ndipo Uri anabereka Bezaleli.
21 Patapita nthawi, Hezironi anagona ndi mwana wamkazi wa Makiri abambo ake a Giliyadi (iye anamukwatira ali ndi zaka 60) ndipo anamuberekera Segubu. 22 Segubu anabereka Yairi, amene anali ndi mizinda 23 ku Giliyadi. 23 (Koma Gesuri ndi Aramu analanda Havoti Yairi komanso Kenati ndi madera ake onse ozungulira, mizinda makumi asanu ndi umodzi). Onsewa anali adzukulu, a Makiri abambo ake a Giliyadi.
24 Atamwalira Hezironi ku Kalebe Efurata, Abiya mkazi wa Hezironi anamuberekera Asihuri abambo a Tekowa.
Yerahimeeli Mwana wa Hezironi
25 Ana a Yerahimeeli, mwana woyamba wa Hezironi anali:
Ramu, mwana wake woyamba, Buna, Oreni, Ozemu ndi Ahiya. 26 Yerahimeeli anali ndi mkazi wina amene dzina lake linali Atara, amene anali amayi a Onamu.
27 Ana a Ramu, mwana woyamba wa Yerahimeeli, anali awa:
Maazi, Yamini ndi Ekeri.
28 Ana a Onamu anali awa:
Shamai ndi Yada.
Ana a Shamai anali awa:
Nadabu ndi Abisuri.
29 Mkazi wa Abisuri anali Abihaili, amene anamuberekera Ahibani ndi Molidi.
30 Ana a Nadabu anali awa:
Seledi ndi Apaimu. Koma Seledi anamwalira wopanda ana.
31 Ana a Apaimu anali awa:
Isi, amene anabereka Sesani.
Sesani anabereka Ahilai.
32 Ana a Yada, mʼbale wa Samai, anali awa:
Yereri ndi Yonatani. Koma Yeteri anamwalira wopanda ana.
33 Ana a Yonatani anali awa:
Peleti ndi Zaza.
Amenewa anali adzukulu a Yerahimeeli.
34 Sesani sanabereke ana aamuna koma aakazi okhaokha.
Iye anali ndi wantchito wa ku Igupto, dzina lake Yariha. 35 Sesani anapereka mwana wake wamkazi kwa Yariha wantchito wake kuti amukwatire ndipo anamuberekera Atayi.
36 Atayi anali abambo ake a Natani,
Natani anali abambo ake a Zabadi,
37 Zabadi anali abambo a Efilali,
Efilali anali abambo a Obedi,
38 Obedi anali abambo a Yehu,
Yehu anali abambo a Azariya,
39 Azariya anali abambo a Helezi,
Helezi anali abambo a Eleasa,
40 Eleasa anali abambo ake a Sisimai,
Sisimai anali abambo a Salumu,
41 Salumu anali abambo a Yekamiya,
Yekamiya anali abambo a Elisama.
Mabanja a Kalebe
42 Ana a Kalebe mʼbale wa Yerahimeeli anali awa:
Mesa mwana wachisamba, anali abambo a Zifi, ndipo mwana wake Maresa anali abambo a Hebroni.
43 Ana a Hebroni anali awa:
Kora, Tapuwa, Rekemu ndi Sema. 44 Sema anali abambo ake Rahamu ndipo Rahamu anali abambo a Yorikeamu. Rekemu anali abambo a Samai. 45 Mwana wa Samai anali Maoni, ndipo Maoni anali abambo a Beti Zuri.
46 Efai, mzikazi wa Kalebe, anali amayi a Harani, Moza ndi Gazezi. Harani anali abambo a Gazezi.
47 Ana a Yahidai anali awa:
Regemu, Yotamu, Gesani, Peleti, Efai ndi Saafi.
48 Maaka mzikazi wa Kalebe anali mayi Seberi ndi Tirihana. 49 Iye anaberekanso Saafi abambo a Madimena ndi Seva abambo a Makibena ndi Gibeya. Mwana wamkazi wa Kalebe anali Akisa. 50 Izi zinali zidzukulu za Kalebe.
Ana a Huri mwana wachisamba wa Efurata anali awa:
Sobala abambo a Kiriati Yearimu, 51 Salima abambo a Betelehemu ndi Harefu abambo ake a Beti-Gadera.
52 Zidzukulu za Sobala abambo a Kiriati Yearimu zinali izi:
Harowe, theka la banja la Manahati, 53 ndipo mabanja a Kiriati-Yeyarimu anali awa: Aitiri, Aputi, Asumati ndi Amisirai. Azorati ndi Aesitaoli anachokera kwa amenewa.
54 Zidzukulu za Salima zinali izi:
Betelehemu, Anetofati, Atiroti-Beti-Yowabu, theka la banja la Manahati, Azori, 55 ndiponso mabanja a alembi amene amakhala ku Yabesi: Atiroti, Asimeati ndiponso Asukati. Awa ndi Akeni amene anachokera kwa Hamati, kholo la Arekabu.
1 Chronicles 2
New International Version
Israel’s Sons(A)
2 These were the sons of Israel:
Reuben, Simeon, Levi, Judah, Issachar, Zebulun, 2 Dan, Joseph, Benjamin, Naphtali, Gad and Asher.
Judah(B)
To Hezron’s Sons
3 The sons of Judah:(C)
Er, Onan and Shelah.(D) These three were born to him by a Canaanite woman, the daughter of Shua.(E) Er, Judah’s firstborn, was wicked in the Lord’s sight; so the Lord put him to death.(F) 4 Judah’s daughter-in-law(G) Tamar(H) bore Perez(I) and Zerah to Judah. He had five sons in all.
5 The sons of Perez:(J)
Hezron(K) and Hamul.
6 The sons of Zerah:
Zimri, Ethan, Heman, Kalkol and Darda[a]—five in all.
7 The son of Karmi:
Achar,[b](L) who brought trouble on Israel by violating the ban on taking devoted things.[c](M)
8 The son of Ethan:
Azariah.
9 The sons born to Hezron(N) were:
Jerahmeel, Ram and Caleb.[d]
From Ram Son of Hezron
10 Ram(O) was the father of
Amminadab(P), and Amminadab the father of Nahshon,(Q) the leader of the people of Judah. 11 Nahshon was the father of Salmon,[e] Salmon the father of Boaz, 12 Boaz(R) the father of Obed and Obed the father of Jesse.(S)
13 Jesse(T) was the father of
Eliab(U) his firstborn; the second son was Abinadab, the third Shimea, 14 the fourth Nethanel, the fifth Raddai, 15 the sixth Ozem and the seventh David. 16 Their sisters were Zeruiah(V) and Abigail. Zeruiah’s(W) three sons were Abishai, Joab(X) and Asahel. 17 Abigail was the mother of Amasa,(Y) whose father was Jether the Ishmaelite.
Caleb Son of Hezron
18 Caleb son of Hezron had children by his wife Azubah (and by Jerioth). These were her sons: Jesher, Shobab and Ardon. 19 When Azubah died, Caleb(Z) married Ephrath, who bore him Hur. 20 Hur was the father of Uri, and Uri the father of Bezalel.(AA)
21 Later, Hezron, when he was sixty years old, married the daughter of Makir the father of Gilead.(AB) He made love to her, and she bore him Segub. 22 Segub was the father of Jair, who controlled twenty-three towns in Gilead. 23 (But Geshur and Aram captured Havvoth Jair,[f](AC) as well as Kenath(AD) with its surrounding settlements—sixty towns.) All these were descendants of Makir the father of Gilead.
24 After Hezron died in Caleb Ephrathah, Abijah the wife of Hezron bore him Ashhur(AE) the father[g] of Tekoa.
Jerahmeel Son of Hezron
25 The sons of Jerahmeel the firstborn of Hezron:
Ram his firstborn, Bunah, Oren, Ozem and[h] Ahijah. 26 Jerahmeel had another wife, whose name was Atarah; she was the mother of Onam.
27 The sons of Ram the firstborn of Jerahmeel:
Maaz, Jamin and Eker.
28 The sons of Onam:
Shammai and Jada.
The sons of Shammai:
Nadab and Abishur.
29 Abishur’s wife was named Abihail, who bore him Ahban and Molid.
30 The sons of Nadab:
Seled and Appaim. Seled died without children.
31 The son of Appaim:
Ishi, who was the father of Sheshan.
Sheshan was the father of Ahlai.
32 The sons of Jada, Shammai’s brother:
Jether and Jonathan. Jether died without children.
33 The sons of Jonathan:
Peleth and Zaza.
These were the descendants of Jerahmeel.
34 Sheshan had no sons—only daughters.
He had an Egyptian servant named Jarha. 35 Sheshan gave his daughter in marriage to his servant Jarha, and she bore him Attai.
36 Attai was the father of Nathan,
Nathan the father of Zabad,(AF)
37 Zabad the father of Ephlal,
Ephlal the father of Obed,
38 Obed the father of Jehu,
Jehu the father of Azariah,
39 Azariah the father of Helez,
Helez the father of Eleasah,
40 Eleasah the father of Sismai,
Sismai the father of Shallum,
41 Shallum the father of Jekamiah,
and Jekamiah the father of Elishama.
The Clans of Caleb
42 The sons of Caleb(AG) the brother of Jerahmeel:
Mesha his firstborn, who was the father of Ziph, and his son Mareshah,[i] who was the father of Hebron.
43 The sons of Hebron:
Korah, Tappuah, Rekem and Shema. 44 Shema was the father of Raham, and Raham the father of Jorkeam. Rekem was the father of Shammai. 45 The son of Shammai was Maon(AH), and Maon was the father of Beth Zur.(AI)
46 Caleb’s concubine Ephah was the mother of Haran, Moza and Gazez. Haran was the father of Gazez.
47 The sons of Jahdai:
Regem, Jotham, Geshan, Pelet, Ephah and Shaaph.
48 Caleb’s concubine Maakah was the mother of Sheber and Tirhanah. 49 She also gave birth to Shaaph the father of Madmannah(AJ) and to Sheva the father of Makbenah and Gibea. Caleb’s daughter was Aksah.(AK) 50 These were the descendants of Caleb.
The sons of Hur(AL) the firstborn of Ephrathah:
Shobal the father of Kiriath Jearim,(AM) 51 Salma the father of Bethlehem, and Hareph the father of Beth Gader.
52 The descendants of Shobal the father of Kiriath Jearim were:
Haroeh, half the Manahathites, 53 and the clans of Kiriath Jearim: the Ithrites,(AN) Puthites, Shumathites and Mishraites. From these descended the Zorathites and Eshtaolites.
54 The descendants of Salma:
Bethlehem, the Netophathites,(AO) Atroth Beth Joab, half the Manahathites, the Zorites, 55 and the clans of scribes[j] who lived at Jabez: the Tirathites, Shimeathites and Sucathites. These are the Kenites(AP) who came from Hammath,(AQ) the father of the Rekabites.[k](AR)
Footnotes
- 1 Chronicles 2:6 Many Hebrew manuscripts, some Septuagint manuscripts and Syriac (see also 1 Kings 4:31); most Hebrew manuscripts Dara
- 1 Chronicles 2:7 Achar means trouble; Achar is called Achan in Joshua.
- 1 Chronicles 2:7 The Hebrew term refers to the irrevocable giving over of things or persons to the Lord, often by totally destroying them.
- 1 Chronicles 2:9 Hebrew Kelubai, a variant of Caleb
- 1 Chronicles 2:11 Septuagint (see also Ruth 4:21); Hebrew Salma
- 1 Chronicles 2:23 Or captured the settlements of Jair
- 1 Chronicles 2:24 Father may mean civic leader or military leader; also in verses 42, 45, 49-52 and possibly elsewhere.
- 1 Chronicles 2:25 Or Oren and Ozem, by
- 1 Chronicles 2:42 The meaning of the Hebrew for this phrase is uncertain.
- 1 Chronicles 2:55 Or of the Sopherites
- 1 Chronicles 2:55 Or father of Beth Rekab
The Word of God in Contemporary Chichewa Copyright © 2002, 2016 by Biblica, Inc.® Used by permission of Biblica, Inc.® All rights reserved worldwide. Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero Mwini © 2002, 2016 ndi Biblica, Inc.® Kugwiritsa ntchito mwachilolezo. Umwini ndi otetezedwa pa dziko lonse.
Holy Bible, New International Version®, NIV® Copyright ©1973, 1978, 1984, 2011 by Biblica, Inc.® Used by permission. All rights reserved worldwide.
NIV Reverse Interlinear Bible: English to Hebrew and English to Greek. Copyright © 2019 by Zondervan.