Add parallel Print Page Options

善惡之較比

不從惡人的計謀,不站罪人的道路,不坐褻慢人的座位,
唯喜愛耶和華的律法,晝夜思想,這人便為有福!
他要像一棵樹,栽在溪水旁,按時候結果子,葉子也不枯乾,凡他所做的,盡都順利。
惡人並不是這樣,乃像糠秕,被風吹散。
因此當審判的時候,惡人必站立不住,罪人在義人的會中也是如此。
因為耶和華知道義人的道路,惡人的道路卻必滅亡。

BUKU LOYAMBA

Masalimo 1–41

Wodala munthu
    amene satsatira uphungu wa anthu ochimwa,
kapena kuyima mʼnjira ya anthu oyipa,
    kapena kukhala mʼmagulu a anthu onyoza.
Koma chikondwerero chake chili mʼmalamulo a Yehova
    ndipo mʼmalamulo akewo amalingaliramo usana ndi usiku.
Iye ali ngati mtengo wodzalidwa mʼmbali mwa mitsinje ya madzi,
    umene umabereka zipatso zake pa nyengo yake
ndipo masamba ake safota.
    Chilichonse chimene amachita amapindula nacho.
Sizitero ndi anthu oyipa!
    Iwo ali ngati mungu
    umene umawuluzidwa ndi mphepo.
Kotero anthu oyipa sadzatha kuyima pa chiweruzo,
    kapena anthu ochimwa mu msonkhano wa anthu olungama.

Pakuti Yehova amayangʼanira mayendedwe a anthu olungama,
    koma mayendedwe a anthu oyipa adzawonongeka.

卷一: 詩篇1—41

有福之人

1-2 不從惡人的計謀,
不與罪人為伍,
不和輕慢上帝的人同流合污,
只喜愛耶和華的律法,
晝夜默誦,
這樣的人有福了!
他就像溪水旁的樹木——
按時結果子,
葉子也不凋零。
他必凡事亨通。
惡人的光景卻截然不同!
他們就像被風吹散的糠秕。
惡人在審判之日必無法逃脫,
罪人在義人的聚會中必站不住腳。
因為耶和華看顧義人的腳步,
惡人的道路必通向滅亡。