丢特腓的恶行

我曾写信给你那里的教会,但喜欢做领袖的丢特腓不理会我们。 10 因此,我若去你们那里,会提及他的所作所为,就是他怎样恶言中伤我们。不仅如此,他还拒绝接待弟兄,并且禁止别人接待,甚至将接待的人赶出教会。

Read full chapter

Za Diotrefe ndi Demetriyo

Ndinalembera mpingo, koma Diotrefe, amene amafuna kukhala wotsogolera, sanafune kutimvera. 10 Tsono ndikabwera ndidzakumbutsa zimene iye amachita. Iye amafalitsa nkhani zabodza zonena ife. Ndipo sakhutira ndi zimenezo, komanso iyeyo amakana kulandira abale. Komanso amaletsa amene akufuna kutero, ndipo amawachotsa mu mpingo.

Read full chapter

I wrote to the church, but Diotrephes, who loves to be first, will not welcome us. 10 So when I come,(A) I will call attention to what he is doing, spreading malicious nonsense about us. Not satisfied with that, he even refuses to welcome other believers.(B) He also stops those who want to do so and puts them out of the church.(C)

Read full chapter