1 Mbiri 7
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
Fuko la Isakara
7 Ana a Isakara anali awa:
Tola, Puwa, Yasubu ndi Simironi ndipo onse analipo anayi.
2 Ana a Tola ndi awa:
Uzi, Refaya, Yerieli, Yahimai, Ibisamu ndi Samueli. Awa anali atsogoleri a mabanja awo. Pa nthawi ya ulamuliro wa Davide zidzukulu za Tola zomwe zinali anthu odziwa kumenya nkhondo zinalipo 22,600.
3 Mwana wa Uzi anali
Izirahiya.
Ana a Izirahiya anali:
Mikayeli, Obadiya, Yoweli ndi Isiya. Onse asanu anali atsogoleri a mabanja. 4 Monga mwa chiwerengero cha mabanja awo, panali anthu 36,000 odziwa kumenya nkhondo, pakuti iwo anali ndi akazi ndi ana ambiri.
5 Abale awo onse a mʼbanja la Isakara amene anali odziwa kumenya nkhondo analipo 87,000, olembedwa potsata mibado yawo.
Fuko la Benjamini
6 Ana atatu a Benjamini anali awa:
Bela, Bekeri ndi Yediaeli.
7 Ana a Bela anali awa:
Eziboni, Uzi, Uzieli, Yerimoti ndi Iri. Iwowa anali atsogoleri a mabanja awo ndipo onse pamodzi analipo asanu. Pa mndandanda wa mʼbado wawo panali anthu 22,034 odziwa kumenya nkhondo.
8 Ana a Bekeri anali awa:
Zemira, Yowasi, Eliezara, Eliyoenai, Omiri, Yeremoti, Abiya, Anatoti ndi Alemeti. Onsewa anali ana a Bekeri. 9 Pa mndandanda wa mʼbado wawo panali atsogoleri a mabanja ndi anthu 20,200 odziwa kumenya nkhondo.
10 Mwana wa Yediaeli anali
Bilihani.
Ana a Bilihani anali awa:
Yeusi, Benjamini, Ehudi, Kenaana, Zetani, Tarisisi ndi Ahisahara. 11 Ana onsewa a Yediaeli anali atsogoleri a mabanja. Analipo anthu 17,200 amene anali okonzeka kupita ku nkhondo.
12 Asupi ndi Ahupi anali zidzukulu za Iri, ndipo Ahusimu anali zidzukulu za Aheri.
Fuko la Nafutali
13 Ana a Nafutali anali awa:
Yahazieli, Guni, Yezeri ndi Salumu, zidzukulu za Biliha.
Fuko la Manase
14 Ana a Manase anali awa:
Asirieli ndi mwana amene anabereka kwa mzikazi wake wa ku Aramu. Mzikazi yemweyo anaberekanso Makiri abambo ake a Giliyadi. 15 Makiri anatenga mkazi wa banja la Ahupi ndi Asupi. Mlongo wake anali Maaka.
Mwana wake wina anali Zelofehadi, amene anabereka ana aakazi okhaokha.
16 Maaka mkazi wa Makiri anabereka mwana wamwamuna ndipo anamutcha Perezi. Mʼbale wake anamutcha Seresi, ndipo ana ake anali Ulamu ndi Rakemu.
17 Mwana wa Ulamu anali
Bedani.
Awa anali ana a Giliyadi mwana wa Makiri, mwana wa Manase. 18 Mlongo wake Hamoleketi anabereka Isihodi, Abiezeri ndi Mahila.
19 Ana a Semida anali:
Ahiyani, Sekemu, Likihi ndi Aniyamu.
Fuko la Efereimu
20 Ana a Efereimu anali awa:
Sutela, Beredi,
Tahati, Eliada,
Tahati, 21 Zabadi,
Sutela.
Ezeri ndi Eladi anaphedwa ndi anthu a ku Gati, pamene anabwera kudzalanda zoweta zawo. 22 Efereimu, abambo awo, anawalira masiku ambiri, ndipo abale ake anabwera kudzamutonthoza. 23 Kenaka anagona ndi mkazi wake, ndipo anakhala woyembekezera nabala mwana wamwamuna. Anamutcha dzina lake Beriya, chifukwa tsoka linagwera banja lake. 24 Mwana wake wamkazi anali Seera, amene anamanga mzinda wa Beti-Horoni Wakumunsi, Wakumtunda kudzanso Uzeni-Seera.
25 Mwana wina wa Efereimu anali Refa amene zidzukulu zake zinali Resefu,
Tela, Tahani,
26 Ladani, Amihudi,
Elisama, 27 Nuni
ndi Yoswa.
28 Malo amene ankakhala anali Beteli ndi midzi yozungulira, cha kummawa kunali Naarani, Gezeri ndi midzi yake ya kumadzulo ndi Sekemu ndi midzi yake mpaka ku Aya ndi midzi yake. 29 Mʼmbali mwa malire a Manase munali Beti-Seani, Taanaki, Megido ndi Dori, pamodzi ndi midzi yake. Zidzukulu za Yosefe mwana wa Israeli zimakhala mʼmizinda imeneyi.
Fuko la Aseri
30 Ana a Aseri anali awa:
Imuna, Isiva, Isivi ndi Beriya. Mlongo wawo anali Sera.
31 Ana a Beriya anali awa:
Heberi ndi Malikieli amene anabereka Birizaiti.
32 Heberi anabereka Yafuleti, Someri, Hotamu ndi Suwa, mlongo wawo.
33 Ana a Yafuleti anali awa:
Pasaki, Bimuhali ndi Asivati.
Awa anali ana a Yafuleti.
34 Ana a Someri anali awa:
Ahi, Rohiga, Yehuba ndi Aramu.
35 Ana a mʼbale wake Helemu anali awa:
Zofa, Imuna, Selesi ndi Amali.
36 Ana a Zofa anali awa:
Suwa, Harineferi, Suwali, Beri, Imula, 37 Bezeri, Hodi, Sama, Silisa, Itirani ndi Bera.
38 Ana a Yeteri anali awa:
Yefune, Pisipa ndi Ara.
39 Ana a Ula anali awa:
Ara, Hanieli ndi Riziya.
40 Onsewa anali zidzukulu za Aseri, atsogoleri a mabanja, anthu omveka, ankhondo olimba mtima, ndi akuluakulu pakati pa atsogoleri anzawo. Chiwerengero cha anthu odziwa kumenya nkhondo chomwe chinalembedwa chinali 26,000.
历代志上 7
Chinese Contemporary Bible (Simplified)
以萨迦的后裔
7 以萨迦的四个儿子是陀拉、普瓦、雅述和伸仑。 2 陀拉的儿子是乌西、利法雅、耶勒、雅买、易伯散和示姆利,他们都是陀拉宗族的族长。在大卫执政年间,陀拉家共有两万二千六百个英勇的战士。 3 乌西的儿子是伊斯拉希。伊斯拉希的儿子是米迦勒、俄巴底亚、约珥、伊示雅,他们五人都是族长。 4 他们妻儿众多,因此各宗族中可以出征作战的共有三万六千人。 5 按家谱的记载,以萨迦支派的各族中共有八万七千个英勇的战士。
便雅悯的后裔
6 便雅悯的三个儿子是比拉、比结和耶叠。 7 比拉的五个儿子是以斯本、乌西、乌薛、耶利摩和以利,他们都是族长,是英勇的战士。按家谱记载,他们宗族共有两万二千零三十四个战士。 8 比结的儿子是细米拉、约阿施、以利以谢、以利约乃、暗利、耶利摩、亚比雅、亚拿突和亚拉篾。 9 比结的儿子都是族长。按家谱的记载,他们宗族共有两万零二百个英勇的战士。 10 耶叠的儿子是比勒罕,比勒罕的儿子是耶乌斯、便雅悯、以忽、基拿拿、细坦、他施和亚希沙哈。 11 这些耶叠的儿子都是族长,宗族中可以英勇作战的共一万七千二百人。 12 以珥的儿子是书品和户品,亚黑的儿子是户伸。
拿弗他利的后裔
13 拿弗他利的儿子是雅薛、沽尼、耶色和沙龙。他们都是辟拉的后代。
玛拿西的后裔
14 玛拿西的妾是亚兰人,她给玛拿西生的儿子是亚斯列,另外还生了基列的父亲玛吉。 15 玛吉娶了户品和书品的妹妹玛迦。玛拿西的次子名叫西罗非哈,西罗非哈只有几个女儿。 16 玛吉的妻子玛迦生了一个儿子,给他取名叫毗利施。毗利施的兄弟名叫示利施,示利施的儿子是乌兰和利金。 17 乌兰的儿子是比但。这些都是基列的子孙。基列是玛吉的儿子,玛吉是玛拿西的儿子。 18 基列的妹妹哈摩利吉生了伊施何、亚比以谢和玛拉。 19 示米大的儿子是亚现、示剑、利克希和阿尼安。
以法莲的后裔
20 以法莲的后代有书提拉,书提拉的儿子是比列,比列的儿子是他哈,他哈的儿子是以拉大,以拉大的儿子是他哈, 21 他哈的儿子是撒拔,撒拔的儿子是书提拉。以法莲的另外两个儿子以谢和以列因为偷迦特人的牲畜而被当地人杀死了。 22 他们的父亲以法莲为他们悲伤了多日,亲戚都来安慰他。 23 后来,以法莲与妻子同房,妻子怀孕,生了一个儿子。以法莲因家里遭遇不幸,就给孩子取名叫比利亚[a]。 24 以法莲有一个女儿叫舍伊拉,她建了上伯·和仑、下伯·和仑和乌羡·舍伊拉。 25 比利亚的儿子是利法和利悉,利悉的儿子是他拉,他拉的儿子是他罕, 26 他罕的儿子是拉但,拉但的儿子是亚米忽,亚米忽的儿子是以利沙玛, 27 以利沙玛的儿子是嫩,嫩的儿子是约书亚。 28 以法莲人的地业和住处包括伯特利及其四围的村庄、东部的拿兰、西部的基色及其四围的村庄、示剑及其四围的村庄,远至迦萨及其四围的村庄。 29 玛拿西人的地业包括伯·善、他纳、米吉多、多珥以及它们四围的村庄。这些是以色列之子约瑟的后代居住的地方。
亚设的后裔
30 亚设的儿子是音拿、亦施瓦、亦施韦、比利亚,女儿是西拉。 31 比利亚的儿子是希别和玛结,玛结的儿子是比撒威。 32 希别的儿子是雅弗勒、朔默、何坦,女儿是书雅。 33 雅弗勒的儿子是巴萨、宾哈和亚施法。这三人是雅弗勒的儿子。 34 朔默的儿子是亚希、罗迦、耶户巴和亚兰。 35 朔默的兄弟希连的儿子是琐法、音那、示利斯和亚抹。 36 琐法的儿子是书亚、哈尼弗、书阿勒、比利、音拉、 37 比悉、河得、珊玛、施沙、益兰、比拉。 38 益帖的儿子是耶孚尼、毗斯巴、亚拉。 39 乌拉的儿子是亚拉,汉尼业和利谢。 40 这些都是亚设的后代。他们都是族长,是英勇的战士和杰出的首领。按照家谱的记载,他们宗族中可以出征作战的共有两万六千人。
Footnotes
- 7:23 “比利亚”意思是“不幸”。
1 Chronicles 7
New International Version
Issachar
7 The sons of Issachar:(A)
Tola, Puah,(B) Jashub and Shimron—four in all.
2 The sons of Tola:
Uzzi, Rephaiah, Jeriel, Jahmai, Ibsam and Samuel—heads of their families. During the reign of David, the descendants of Tola listed as fighting men in their genealogy numbered 22,600.
3 The son of Uzzi:
Izrahiah.
The sons of Izrahiah:
Michael, Obadiah, Joel and Ishiah. All five of them were chiefs. 4 According to their family genealogy, they had 36,000 men ready for battle, for they had many wives and children.
5 The relatives who were fighting men belonging to all the clans of Issachar, as listed in their genealogy, were 87,000 in all.
Benjamin
6 Three sons of Benjamin:(C)
Bela, Beker and Jediael.
7 The sons of Bela:
Ezbon, Uzzi, Uzziel, Jerimoth and Iri, heads of families—five in all. Their genealogical record listed 22,034 fighting men.
8 The sons of Beker:
Zemirah, Joash, Eliezer, Elioenai, Omri, Jeremoth, Abijah, Anathoth and Alemeth. All these were the sons of Beker. 9 Their genealogical record listed the heads of families and 20,200 fighting men.
10 The son of Jediael:
Bilhan.
The sons of Bilhan:
Jeush, Benjamin, Ehud, Kenaanah, Zethan, Tarshish and Ahishahar. 11 All these sons of Jediael were heads of families. There were 17,200 fighting men ready to go out to war.
12 The Shuppites and Huppites were the descendants of Ir, and the Hushites[a] the descendants of Aher.
Naphtali
Manasseh
14 The descendants of Manasseh:(E)
Asriel was his descendant through his Aramean concubine. She gave birth to Makir the father of Gilead.(F) 15 Makir took a wife from among the Huppites and Shuppites. His sister’s name was Maakah.
Another descendant was named Zelophehad,(G) who had only daughters.
16 Makir’s wife Maakah gave birth to a son and named him Peresh. His brother was named Sheresh, and his sons were Ulam and Rakem.
17 The son of Ulam:
Bedan.
These were the sons of Gilead(H) son of Makir, the son of Manasseh. 18 His sister Hammoleketh gave birth to Ishhod, Abiezer(I) and Mahlah.
19 The sons of Shemida(J) were:
Ahian, Shechem, Likhi and Aniam.
Ephraim
20 The descendants of Ephraim:(K)
Shuthelah, Bered his son,
Tahath his son, Eleadah his son,
Tahath his son, 21 Zabad his son
and Shuthelah his son.
Ezer and Elead were killed by the native-born men of Gath, when they went down to seize their livestock. 22 Their father Ephraim mourned for them many days, and his relatives came to comfort him. 23 Then he made love to his wife again, and she became pregnant and gave birth to a son. He named him Beriah,[c] because there had been misfortune in his family. 24 His daughter was Sheerah, who built Lower and Upper Beth Horon(L) as well as Uzzen Sheerah.
25 Rephah was his son, Resheph his son,[d]
Telah his son, Tahan his son,
26 Ladan his son, Ammihud his son,
Elishama his son, 27 Nun his son
and Joshua his son.
28 Their lands and settlements included Bethel and its surrounding villages, Naaran to the east, Gezer(M) and its villages to the west, and Shechem and its villages all the way to Ayyah and its villages. 29 Along the borders of Manasseh were Beth Shan,(N) Taanach, Megiddo and Dor,(O) together with their villages. The descendants of Joseph son of Israel lived in these towns.
Asher
30 The sons of Asher:(P)
Imnah, Ishvah, Ishvi and Beriah. Their sister was Serah.
31 The sons of Beriah:
Heber and Malkiel, who was the father of Birzaith.
32 Heber was the father of Japhlet, Shomer and Hotham and of their sister Shua.
33 The sons of Japhlet:
Pasak, Bimhal and Ashvath.
These were Japhlet’s sons.
34 The sons of Shomer:
Ahi, Rohgah,[e] Hubbah and Aram.
35 The sons of his brother Helem:
Zophah, Imna, Shelesh and Amal.
36 The sons of Zophah:
Suah, Harnepher, Shual, Beri, Imrah, 37 Bezer, Hod, Shamma, Shilshah, Ithran[f] and Beera.
38 The sons of Jether:
Jephunneh, Pispah and Ara.
39 The sons of Ulla:
Arah, Hanniel and Rizia.
40 All these were descendants of Asher—heads of families, choice men, brave warriors and outstanding leaders. The number of men ready for battle, as listed in their genealogy, was 26,000.
Footnotes
- 1 Chronicles 7:12 Or Ir. The sons of Dan: Hushim, (see Gen. 46:23); Hebrew does not have The sons of Dan.
- 1 Chronicles 7:13 Some Hebrew and Septuagint manuscripts (see also Gen. 46:24 and Num. 26:49); most Hebrew manuscripts Shallum
- 1 Chronicles 7:23 Beriah sounds like the Hebrew for misfortune.
- 1 Chronicles 7:25 Some Septuagint manuscripts; Hebrew does not have his son.
- 1 Chronicles 7:34 Or of his brother Shomer: Rohgah
- 1 Chronicles 7:37 Possibly a variant of Jether
The Word of God in Contemporary Chichewa Copyright © 2002, 2016 by Biblica, Inc.® Used by permission of Biblica, Inc.® All rights reserved worldwide. Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero Mwini © 2002, 2016 ndi Biblica, Inc.® Kugwiritsa ntchito mwachilolezo. Umwini ndi otetezedwa pa dziko lonse.
Chinese Contemporary Bible Copyright © 1979, 2005, 2007, 2011 by Biblica® Used by permission. All rights reserved worldwide.
Holy Bible, New International Version®, NIV® Copyright ©1973, 1978, 1984, 2011 by Biblica, Inc.® Used by permission. All rights reserved worldwide.
NIV Reverse Interlinear Bible: English to Hebrew and English to Greek. Copyright © 2019 by Zondervan.